Wapangodya FANS

Wapangodya FANS God is Good

13/07/2025

May God meet your needs so that you can help your family, relatives and friends in Jesus name Amen.

15/10/2024

Kwa onse amayi anu anakali nd moyo happy mother's day to them. Kwa enafe amene anatsogola Ku ulemelero MTSCRIP

07/12/2022

Hello guys.. You're welcome to this group. As one family, feel free to speak out and share what God has made us see His glory from old terrible days/ hours of life. Ine ndangolandra kumene bachelor's degree in secondary education last month 19..... Share yours guys

22/09/2022

MAU A CHITSITSIMUTSO

MUSAKUMBUKIRE ZAKALE
----------------------------------------
📖 Yesaya 43:18 Musakumbukire zidapitazo, ngakhale kulingalira zinthu zakale.

AMEN MPINGO

Abale ndi Alongo; ena kale lathu ndi lolilitsa lomwe timati tikakumbukira nyengo zomwe timadutsa, misozi imatuluka koma mau a Mulungu ak*ti musakumbukire zakale kapena kulingalira koma pemphero lathu lidzikhala lak*ti Mulungu chitani chatsopano pa moyo wanga mu dzina la Ambuye Yesu Khristu

mwadutsa mu zotani kale lanu?

adakusiyani banja mwachipongwe ndi mochititsa manyazi musakumbukire zakale chonde koma Mulungu akupatseni zatsopano

Kudachitika chani kale lanu?

Adakuonongerani Business, kapena adakuonogerani ndalama zomangira nyumba, kapena adakuchotsetsani ntchito kapena adakupherani wachibale mu njira zamatsenga, musalingalire zimenezo kapena musakumbukire koma pemphero lanu likhale lak*ti Ambuye Yesu Khristu achite zatsopano.

Kale lanu lidali lotani?

Mwakula pa umasiye ndipo okhala nawo amkakuzuzani kapena adakukanani k*ti sangakhale nanu kapena mwakula mu umphawi chonde musakumbukire zakale pempherani k*t Ambuye Yesu achite chatsopano

Chidachitika mchani kale lanu? amkakunenani k*ti ndinu opanda ntchito, opanda mzeru, osakongola, osaoneka bwino kapena adakunyozani mochititsa manyazi, chonde musakumbukire zakale

Kukumbukira kwambiri zakale kumapangitsa munthu kumangodandaula, mwinaso zinthu zomwe mukudandaulazo ndi zak*ti sizingabwerereso; koma Mulungu amatha kuchibwezeretsa chimenecho mu njira ina ngati tikupemphera k*ti achite chatsopano ndipo Mulungu sachita chatsopano chifukwa tikudandaula; koma tikupemphera choncho langizo langa ku mpingo ndilak*t tizipemphera k*ti Mulungu achite chatsopano

Chonde musalingalire zakale zidapita zimenezo koma pempherani k*ti AMBUYE YESU KHRISTU achite zatsopano

Mulungu akudalitseni ndi mtima oiwala zowawa zakale mu dzina la Ambuye Yesu Khristu

AMEN AMEN AMEN AMEN

22/09/2022

Bambo wina emwe anali ndi chuma chochuluka kunyumba kwake akuweluka ku
ntchito anayimitsa galimoto lake pafupi ndi
ATM pa Bank k*ti atape ndalama
Atawona k*ti pa ATM panalibe aliyense anangosiya galimoto lake likulira iye
ndik*tuluka kukatapa khobiri. Posakhalitsa
munthu wina anangolowa m'galimotolo
nathawa nalo
Bamboyi anayesa k*tumiza
mauthenga ku police ndi pa wailesi koma sizinaphule kanthu, galimoto silinapezeke
Tsiku lina akuweluka kuntchito
anangodabwa galimoto lake losowa lija liri
panja pa mpanda wake. Linali bwino lomwe
popanda pokandika paliponse. Atatsekula
chitseko mkati anapezamo kalata
yolembedwa motere...
Pepa m'bale wanga.
Sichinali cholinga changa kukubera galimoto lako koma ndimathamangira kuchipatala
ndiye simkanachitira mwina. Ndadziwa
komwe umakhala chifukwa cha mapepala
ako omwe ndinawapeza m'galimotoli.
M'malo mwake ngati kupepesa ndakalipira
ku hotel yapamwamba k*ti iwe ndi banja
lako mawa mukasangalare, ma tikiti
ndawasiya mgalimoto lomweri pasi pa mpando
Bamboyi atawona izi anawuza
mkazi wake monga momwe zakhalira.
Mawa lake banja lonse linatengana waku
hotel kukasangalala. Atasangalarasangalara
pamene amafika ku nyumba zachisoni
anapeza katundu ense okwanira chuma
chankhaninkhani atabedwa
Anangopeza kakalata potelo katalembedwa
k*ti...Nditawona chuma chomwe uli nacho
muma pepala ndinawepeza mgalimoto lako
ndinawona k*ti kuli bwino kusiya galimoto
ndikudzaba chuma chako cha mnyumba pamene iwe uli ku
hote. Bambo anazungizika mutu..
Ndi chimodzimodzinso momwe aliri satana...
Atawona zabwino zomwe
anatikozera sanje inamkulira... Ndi chifukwa
chake lero lino amabwera ngati zabwino
iwe ndikumati bola pamenepa osadziwa ndi
msampha ok*tengera ku chiwonongeko.
Yohane 8: 44 akunenetsa k*ti satana ndi tate wa bodza ndipo mwa iye mulibe
chowona. Usanyengeke m'bale wanga ndi zamdziko pak*ti ndizotsala.
yang'ana kwa Mulungu ndiye kuli
moyo..

Amen!!

18/09/2022

I walked into a hotel and after going through the menu, I ordered some food. After about 20 mins a group of guys and ladies walked in & ordered theirs. To my dismay, these folks got served first. I watched as they began to eat& laugh heartily. I even overheard one of them bragging about how connected he is to everyone in the hotel and I felt mocked . I decided to leave. Unable to take it anymore , I called the waiter. He calmly told me: "yours is a special order, being prepared by the chief chef himself. Their orders were prepared hurriedly by students on industrial attachment because the top chefs are busy with yours Sir. That's why they were served first. Please have some juice as you wait". I calmed down & waited patiently.
Shortly after, my meal was served by 6 waiters. Unknown to me, the owner of the hotel (who happened to be an old long lost friend of mine) saw me when I entered and decided to surprise me. She changed my simple meal to a five-star meal. The party at the other table were shocked. They couldn't stop staring. Suddenly they were the ones murmuring, asking why they didn't get that kind of service and meal.
Such is life! Some people are ahead of you and are eating now, laughing at you and talking about how they are smarter, wiser and better than you, how they are well connected, blessed, have money and are enjoying life . You are waiting tirelessly wondering why it's taking so long to breakthrough, You endure mockery and humiliation. Maybe you have contemplated su***de, gone throughout depression or suffered severe mental anxiety. Do not worry! The owner of the world has seen u & doesn't want u to be served a simple meal like those making a mockery of you. You're waiting long because yours is a special meal. It takes time to prepare. And only chief chefs prepare them.
Wait for your meal and relax . When it comes that laughing party will be silenced for good.
Stay Blessed

18/09/2022

Ngakhale satana wamwaza ma agent ake mdzikoli monga asing'anga k*ti athandize anthu nkhani yachuma, matenda, mabanja, ndi zina zambiri poona mavuto omwe tikudutsamo, chonde mbale wanga tisakopeke amenewa ndi matchera.

Satana kwake ndi kuba ,kupha ndi kuononga. Eksodo 20:3 ak*ti; musakhale nayo milungu ina koma Ine ndekha.
Yehova safuna kumusakaniza,anatuma mwana wake kudzatizindikilitsa zamphavu yake. Mwa Iye muli zonse tizisowa.

Satana ndi ochenjera, amafuna kupikisana ndi Mulungu wakumwamba chosecho adagonjetsedwa kale. Adamuthamangitsa kumwamba kamba kodzikuza. Musamuvere ndi wabodza mboni ndi Adamu ndi Hava adawanamiza ndikuchimwa. Lero ali pakati pathu,ali ndi maso auzimu akuona samalani.

Nde pano walowa mmipingo ndi zozizwa, kugwiritsa ntchito a prophet, abusa ndi ena ,inu mkumati zilibwino. Safuna kugona satana poti nthawi yamuthera k*ti akaweruzidwe, 2 Atesalonika 2:1-12

Muwerenge mofatsa bwino buku limeneri mudziwa choona pomwe satana akupezeka pano. Werenganiso mabuku awa, 2 Akorinto 6: 14 -18 komaso Chibvumbulutso 18:1-5 God bless you.

12/09/2022

KOMA PALIBE CHIDZATILEKANITSA😭
M'Mudzi winawake munali kukhala anthu ambiri, koma unali mudzi wa malamulo, ndipo anthu onse anali ogwirizana.
Ndiye amfumu a mmudzimo anali atalamula k*ti: "Sitifuna kumva ndi kuona k*ti wina wa mmudzi muno ndi mkristu, ndipo akadzayerekeza munthu wina k*tsatira chikristu adzalira kwambiri".
Ndipo iyi inali lamulo lamphamvu ndiponso loopsa, ndipo anthu onse amayenera kuitsatira lamuloli, ndipo tsiku lina munthu wina anapezedwa akupemphera mnyumba mwake, koma anthu ena anamnenera kwa olamulira ndipo anamugwira ndi kumupha, izi zinapereka mantha kwa anthu ena amene anali akristu.

Ndiye mkati mwa mudzi muja munali munthu wina amene ankalalikira Uthenga, ndipo analalikira Uthenga kwa anthu osiyanasiyana.
Ndipo banja linalake linatembenuka mtima, ndipo onse anali kumasonkhana kunyumba inayake Koma zinali zopatsa mantha kwambiri, chifukwa mfumu inali itakwiya kwambiri, ndipo tsiku lina anagwidwa mmodzi wa mgulu lija la akristu, ndipo anamumenya ndi kumupachika, ndipo anapachikanso chikwangwani cholembedwa k*ti: "Winanso Ayerekeze kupanga zosakhala bwino apachikidwenso".
Izi zinapereka chiopsezo kwa okhulupirira ena, ndipo ambiri anayamba k*taya mtima, ndipo ankadzifunsa k*ti: "Kodi ndi liti tidzapeze mtendere ife"?😭😭
Okhulupirira anadandaula kwambiri, Koma Mlaliki uja anawauza k*ti: "Mukudziwa, moyo wachikristu nd moyo wowawitsa kwambiri, koma tiyeni tiiwale zakumbuyo, koma tiganize zak*tsogolo, tiyeni tipirire koma tikhale chifupi ndi chiyembekezo chathu mwa Kristu Yesu, pak*ti ngati ine ndi inu Yesu adatikonda ndipo anatifera natitenga, Palibe angatichotse mmanja mwake, palibe amene angatisiyanitse ndi chikondi chake, Koma tilimbe pak*ti ngakhale masautso tikudutsawa sangatisiyanitse ndi chikondi cha Yesu Kristu"🙏.
Anthu aja atamva mauwa analimbika mtima kupirira mmayesero onse, ndipo anali okonzeka k*tonzedwa chifukwa Cha Yesu Kristu, Ndipo patsogolo pake anthu aja anadzionetsera poyera, ndipo anayamba kumabvomereza poyer

09/09/2022

ABWENZI APA DZIKO

Panali pakati pa usiku pomwe mwana wanga anadwala mwa kayakaya.
Mutu wanga unaima kulingalira k*ti ndiyenda naye bwanj kukafika kuchipatala popeza ndalama ndinalibe.

Ndinayesa kubwereka ndalama kwa neba wanga koma iye adati ndalama ndilibe.

Ndinayesa kuimbila phone azibale anga k*ti andithandize koma onse anati tione mawa kukacha

Ndinayesa kuyimbila phone azinzanga aku ntchito ndi ena apa facebook k*ti andithandize koma onsewo ankangoti ndilibe ndilibe. Komanso ena samandiyankha nkomwe, ankangondidyesa ma blue tick.

Ndinaimbira phone abwana anga ku ntchito k*ti andithandize koma iwo anati mubwere mawa ku office k*ti muzasayine form.

Kenako ndinaona k*ti ndikuchedwa nditha kuluza moyo wa mwana. Ndinangom'beleka mwanayo nkuyamba k*thamanga naye wakuchipatala wapansi.

Koma zachisoni, ndili mu nsewu ndinadabwa kuona k*ti mwana uja waumisa khosi wasiya kugwedera or kupuma.
Apa mpamene ndinadziwa k*ti chinachake chachitika, komabe ndinazilimbitsa mtima mpaka ndinakafika kuchipatala kuja misozi ikusika m'masaya mwanga😭

Adotolo atangomugwira mwanayo adandiyang'ana nkupukusa mutu amvekere "pepani mwana watisiya kale uyu" oooooooh ndinalira😭😭😭

Azibale anga omwe amati alibe ndalama aja atamva uthenga wamaliro anabwera ndi galimoto kuzanyamula thupilo.

Abwana omwe amati ndipite ku office aja anabwera kuzandipasa ndalama zankhani nkhani ngati chipepeso opandaso ku sign form.

Azinzanga apa facebook omwe amandidyesa ma blue tick aja kunali kuika ma status a Rest in peace rest in peace.

Neba wanga amene amati ndalama alibe uja anandipepesa ndi ndalama zankhani nkhani.

Ndinazimvera chisoni kuona chithandizo chikubwera pa Nthawi yomwe mwana wanga saamafunikira

Abale anga okondeka dziwani izi : Abwenzi omwe tili nawowa amaonetsa chikondi pa Nthawi yomwe wasiya kupuma.Uli moyo utha kuvutika ndikuvutika opanda olo m'modzi wok*thandiza.

Koma pali m'mozi yemwe amakhala nafe Nthawi zonse ameneyo ndiye YESU🙏

Hallelujah!

06/09/2022

A Rich man looked through his
window and saw a man picking
something from his dustbin. He
said, Thank GOD I'm not poor.
The poor man looked around
and saw a naked man
misbehaving on the street. He
said, Thank GOD I'm not mad.
The mad man looked ahead and
saw an ambulance carrying a
patient. He said, Thank GOD am
not sick.
Then a sick person in hospital
saw a trolley taking a dead body
to the mortuary. He said, Thank
GOD I'm not dead.
Only a dead person can not
thank God (Psalm 115:17). Why
don't you thank GOD today for
giving you the opportunity to live
another day?
Would you share with someone
else, and let them know that God
loves them too?

I don’t know why people skip posts about God but if you are not among those who skip God the say this prayer

LORD GOD FATHER,
Today I have so many things to thank you for. especially for this wonderful day. I thank you for my parents, my children, my brothers, my family members, my workers, my neighbors, my clients, my supplier, my creditors, my debtors, my friends and for all the people who cross my path, and how everything is yours LORD, I pray o:
God bless me.
God bless my life.
May God bless my health.
God bless my heart
May God bless my home.
God bless my family.
God bless my work
May God bless my spiritual life.
God bless my finances.
God bless all my projects.
May God bless me and my family in abundance.
Just as water falls from the sky, so the greatest blessings will fall on you... in the name of Jesus Christ of Nazarene!!!
I repeat: ′′ JESUS you are my strength, I need you, heal me and heal my family and the whole world.

If you have read to the end, Use 60 SECONDS Share this Message in 5 different prayer groups!
Soon you will have made countless people pray to God for each other.
So sit back and watch the power of God
Working in your life
Don’t ignore

lcan'tIgnoreGod

EndTimeGen
-------------------

21/08/2022

My fellow Wapangodya fans, we welcome you to this page where testimonies of inspiration are shared, share how you turned to be wapangodya after rejection.

17/08/2022

NKHANI YONVETSA CHISONI YABAMBO YEMWE MUKUMUONAYI ADALUMIKIZITSIDWA KUZIDOLO KOMA M'MATSENGA.

Kungoyambira pachinyamata changa, moyo wanga wakhala osanvetsetseka maningana ndizomwe ndakhala ndikukumana nazo.
Ndimati ndikapeza kachibwezi, sindimatha chaka chisanathepo koma ine osalakwa.
Nthawi zambiri ndimakhala ndikukhumudwitsidwa koma vuto langa osalipeza.

Mpaka ndinafika pongo giver basi k*ti mwina zazibwezi simbali yathu. Zinalibe zovuta pauchinyamata kukhala opanda wachikondi. Ma friends ndi anthu ena okuzungulira nkhani imakhala yako. Komabe nanga ndidakatani popeza ndimakholalira kukhumudwitsidwa.

Ndinakula mpaka 34 years koma opanda mkazi. Ndinakhala pafupifupi kwazaka 5 osaipeza ntchito. Chirichonse sichimandiyendera ndipo ndimangosowa mtendere ndikamakhala nkumazifusa k*ti kwenikweni ine vuto ndichani?

Ndinapeza ntchito mwamwayi yomasesa komanso kukolopa ku restaurant ndipo ndinalidi ozipereka ndipo ndimailemekeza ntchito yanga. Ngakhale ndinali okhulupirika koma salary yanga samandikwezera pamene ena amawakwezera. Pena mpaka ndimatha myezi iwiri osalandira, moti ndimalephera kungoisiya ntchitoyo k*ti nanga ndikaisiya ndilowera k*tiko???

Tsiku lina ndikusesa ndinaona munthu wina wabambo atakhala pa mpando akundikodola. Bamboyo amandiitanira chakudya k*ti tidye limodzi. Ndinayesesa kukana koma anakakamira ndithu mpaka ndinayambadi kudya naye.

Koma tirinkati mokudya muja, adandilakhula nk*ti chifukwa chani ndikuoneka osowa mtendere ndiwankhawa? Ine misozi inayamba kugwa 😭😭😭 ndikuchita kusowa poyamba kuyakhira. Ndirinkati mozinvera chisoni muja, bamboyo adangondiuza k*ti lero ndikaweruka kuntchito ndingopita direct kunyumba kwanga ndipo ndizikapephera mpaka nthawi yoti ndigone ikakwane.

Atangolakhula choncho bamboyo adachokapo ndipo sindithaso kumuona komwe adalowera. Nthawi yowerukira itakwana, ndinayendadi direct wapakhomo panga. Nditafika ndinayambadi kupephera mosweka mtima poona nyengo zowawitsa zomwe ndimadutsamo. Koma zoopsa ndithu ndid

Address

Blantyre

Telephone

+265998080623

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Wapangodya FANS posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Practice

Send a message to Wapangodya FANS:

Share

Share on Facebook Share on Twitter Share on LinkedIn
Share on Pinterest Share on Reddit Share via Email
Share on WhatsApp Share on Instagram Share on Telegram