
23/09/2024
It's worth taking a try
Order your box on 0881074706
*KODI KHANSA YA M'MAWERE IMAYAMBA BWANJI?*
```Azimayi ochuluka akuluza bere tsiku ndi tsiku. Koma kodi cancer imeneyi imayamba bwanji? Imayamba chifukwa cha ma chemicals ochokera ku ma sanitary pads, mankhwala a njira za kulera kapena chlorine yemwe timamwa kudzera ku madzi. Koma oopsa kwambiri ndi ma sanitary pads. Ma pads amenewa omwe mzimayi amavala akamachita periods ali ndi ma chemicals ochedwa dioxins ndi feran. Ma chemicals amenewa amayamwidwa ndi thupi la mzimayi ndipo amalowerera thupi lonse. Ndipo akafika mu chiwindi amasokoneza system ya thupi lonse. Kenako ma hormones amabalalika ndipo chiwindi chimalephera kuteteza thupi ku matenda. Ndipo ma hormones amayamba kugwira ntchito mobalalika, akhoza kulamulira kuti heavy periods, abnormal periods kapena chotupa mchiberekero chiyambike.
Ma hormones a mmabere akabalalika, ma cancer cells nkuyamba kuswana basi mkaka otsalira umayamba kuundana kukhala chotupa zomwe mapeto ake imasanduka cancer.
Ngakhale ku chipatala amayesetsa kuthana ndi cancer mwa njira yochotsa bere kapena chemotherapy, komatu njirazi sizithandiza kwenikweni. Chifukwa zimatheka munthu walandira chemotherapy kapena kumuchotsa bere koma cancer nkumafalikirabe. Njirazi zimakhala ngati angodula mtengo nkusiya muzu ndi chitsa chake. Mapeto ake mtengowo umayambanso kuphuka. Ndi chimodzimodzi ndi kumuchotsa munthu chotupa mchiberekero, chimadzayambanso.
Njira yothana ndi cancer si kudula bere kapena chemotherapy ayi koma kutsuka mu chiwindi kuti chiyambe kugwira bwino ntchito. Izi ndi zomwe Diva Secret Sterm Cell amachita, amatsuka mu chiwindi komanso kuchikonza kuti chiyambenso kugwira bwino ntchito yoteteza ku matenda. Nthenda iliyonse imayamba kuthawa yokha mthupi chiwindi chikayamba kukhala cha thanzi.Paja Diva ndi opanga ma cell amene afa komaso amachotsa poison``` aliyese . *Wakutsina khutu ndi m'nasi*