30/10/2025
A Silvester Ayuba James, Membala wa Chipani cha MCP alemba kuti :
Ku Tanzania inde sizinakhale bwino, koma at least mkazi uja anali ndi plan B. Kupanga eliminate competition. Amadziwa kuti chisankho sichipanganika. Koma adha athu aja kumagwira makhoma ndi mapemphero anzawo akuwaponda ku ma polling center. No plan B, no emergency response plan, no political foresight. Greed basi.
Kenako kumadzalira pa TV eleventh hour, akuti anthu akundilepheretsa kuyendetsa Boma, koma mukandivoteranso ndidzawachotsa chifukwa ndikuwadziwa.
Malabishi!!!
Adha aja ndi panja penipeni. Mwati munakawakumba kutiko kodi?